-
Yeremiya 52:9Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 Kenako Akasidiwo anagwira mfumuyo nʼkupita nayo ku Ribila kwa mfumu ya Babulo mʼdziko la Hamati ndipo anaipatsa chigamulo.
-