-
Ezekieli 1:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 Angelowo ankapita kulikonse kumene mzimu ukufuna kuti apite, kulikonse kumene mzimuwo wapita. Mawilowo ankakwera mʼmwamba limodzi ndi angelowo chifukwa mzimu womwe unkatsogolera angelowo unkatsogoleranso mawilowo.
-