-
Ezekieli 9:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Ndiyeno ndinaona amuna 6 akubwera kuchokera kugeti lakumtunda+ loyangʼana kumpoto, aliyense atanyamula chida chake chowonongera. Pakati pawo panali munthu mmodzi atavala zovala zansalu ndipo mʼchiuno mwake munali kachikwama ka mlembi, konyamuliramo inki ndi zolembera. Anthuwo analowa mkati nʼkuima pambali pa guwa lansembe lakopa.*+
-