-
Ezekieli 18:24Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
24 ‘Munthu amene amachita zinthu zabwino akasiya kuchita zabwinozo nʼkumachita zoipa,* akamachita zinthu zonse zonyansa zimene munthu woipa amachita, kodi angapitirize kukhala ndi moyo? Zinthu zabwino zimene ankachita sizidzakumbukiridwa.+ Iye adzafa chifukwa chochita zinthu mosakhulupirika ndiponso chifukwa cha machimo ake amene anachita.+
-