Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 20:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Koma a nyumba ya Isiraeli anandipandukira mʼchipululu.+ Iwo sanatsatire malamulo anga ndipo anakana zigamulo zanga zimene munthu akamazitsatira, zimamuthandiza kuti akhale ndi moyo. Sabata langa analidetsa kwambiri. Choncho ndinatsimikiza mtima kuti ndiwatsanulire mkwiyo wanga mʼchipululu kuti onse ndiwawonongeretu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena