Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 21:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Koma iwe mwana wa munthu, jambula msewu umene ukuchokera mʼdzikolo. Pamalo ena msewuwo ugawikane nʼkukhala misewu iwiri. Mfumu ya Babulo imene ikubwera ndi lupanga idzasankha msewu umene ikuyenera kudutsa. Pamphambano pamene misewuyi yagawikana uikepo chikwangwani cholozera* kumene kuli mizindayo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena