-
Ezekieli 23:33Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
33 Udzaledzera kwambiri ndipo udzakhala ndi chisoni.
Udzaledzera ndi zinthu zamʼkapu ya mchemwali wako Samariya,
Zinthu zochititsa mantha kwambiri komanso zowononga.
-