-
Ezekieli 24:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 Mʼmawa ndinalankhula ndi anthu ndipo madzulo, mkazi wanga anamwalira. Choncho mʼmawa wa tsiku lotsatira ndinachita zonse zimene anandilamula.
-