-
Ezekieli 26:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Choncho Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Ine ndikuukira iwe Turo ndipo ndikutumizira mayiko ambiri kuti adzamenyane nawe. Iwo adzabwera ngati mafunde amʼnyanja.
-