7 Ine ndikubweretsa anthu ochokera mʼmayiko ena kuti adzakuukire, anthu ankhanza kwambiri a mitundu ina.+
Iwo adzasolola malupanga awo nʼkuwononga chilichonse chokongola chimene unapeza chifukwa cha nzeru zako
Ndipo adzaipitsa ulemerero wako waukulu.+