3 Umuuze kuti: ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti:
“Ine ndikulanga iwe Farao mfumu ya Iguputo,+
Iwe chilombo chachikulu chamʼnyanja chimene chagona mʼngalande zotuluka mumtsinje wake wa Nailo,+
Ndipo wanena kuti, ‘Mtsinje wa Nailo ndi wanga.
Ineyo ndinaupanga ndekha.’+