Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 32:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Iwo amupangira bedi pakati pa anthu amene aphedwa limodzi ndi gulu la anthu ake onse amene ankamutsatira, onse azungulira manda ake. Onsewo ndi anthu osadulidwa, amene aphedwa ndi lupanga chifukwa anachititsa kuti anthu amene akukhala mʼdziko la anthu amoyo azikhala mwamantha. Iwo adzachita manyazi limodzi ndi anthu amene akutsikira kudzenje.* Iye waikidwa mʼmanda pakati pa anthu ophedwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena