Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 32:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Kumeneko kuli akalonga* onse akumpoto limodzi ndi Asidoni onse+ amene anatsikira kumanda ali amanyazi. Anatsikira kumeneko limodzi ndi anthu amene anaphedwa, ngakhale kuti anali ochititsa mantha chifukwa cha mphamvu zawo. Adzagona mʼmanda ali osadulidwa limodzi ndi anthu amene anaphedwa ndi lupanga ndipo adzachita manyazi limodzi ndi anthu amene akutsikira kudzenje.*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena