-
Ezekieli 32:30Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
30 Kumeneko kuli akalonga* onse akumpoto limodzi ndi Asidoni onse+ amene anatsikira kumanda ali amanyazi. Anatsikira kumeneko limodzi ndi anthu amene anaphedwa, ngakhale kuti anali ochititsa mantha chifukwa cha mphamvu zawo. Adzagona mʼmanda ali osadulidwa limodzi ndi anthu amene anaphedwa ndi lupanga ndipo adzachita manyazi limodzi ndi anthu amene akutsikira kudzenje.*
-