Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 41:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mʼmbali zonse za kachisiyo munali masitepe oyenda chozungulira opitira mʼzipinda zamʼmwamba amene ankakulirakulira akamakwera mʼmwamba.+ Zipinda za nsanjika yachitatu zinali zokulirapo kuposa za nsanjika yachiwiri, ndipo zipinda za nsanjika yachiwiri zinali zokulirapo kuposa za nyumba yapansi. Munthu akafuna kupita kuzipinda zamʼmwamba kuchokera kuzipinda zapansi ankadutsa mʼzipinda zapakati.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena