Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 45:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Koma mtsogoleri ndi amene adzakhale ndi udindo woyangʼanira nsembe zopsereza zathunthu,+ nsembe yambewu+ ndi nsembe yachakumwa. Iye azidzayangʼanira nsembezo pa nthawi ya zikondwerero,+ pa masiku amene mwezi watsopano waoneka, pa masiku a Sabata+ ndi pa nthawi ya zikondwerero zonse za nyumba ya Isiraeli.+ Mtsogoleriyo ndi amene azidzapereka kwa ansembe nsembe yamachimo, nsembe yambewu, nsembe yopsereza yathunthu ndi nsembe zamgwirizano kuti aphimbe machimo a nyumba ya Isiraeli.’

  • Ezekieli
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 45:17

      Nsanja ya Olonda,

      3/15/2010, tsa. 26

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena