Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 46:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mtsogoleri wa anthu asamakakamize munthu aliyense kuti achoke pamalo omwe ndi cholowa chake nʼkutenga malowo kuti akhale ake. Ana ake aamuna aziwapatsa cholowa kuchokera pamalo amene ali nawo, kuti pakati pa anthu anga pasapezeke munthu aliyense amene wathamangitsidwa pamalo ake.’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena