Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 48:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Malo amene atsala kumbali zonse za chopereka chopatulika ndiponso ya malo a mzinda akhale a mtsogoleri wa anthu.+ Malowa adzachita malire ndi malo omwe ndi chopereka, amene akukwana mikono 25,000 kumʼmawa ndi kumadzulo. Malowo achite malire ndi malo amene anaperekedwa aja ndipo akhale a mtsogoleri wa anthu. Malo omwe ndi chopereka chopatulika komanso malo opatulika a kachisi aja akhale pakati pa malo a mtsogoleriwa.

  • Ezekieli
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 48:21

      Nsanja ya Olonda,

      9/15/1988, tsa. 27

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena