Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 3:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndiye ngati ndinu okonzeka kugwada nʼkulambira fano lagolide, mukamva kulira kwa lipenga, chitoliro, zeze wamngʼono, zeze wamakona atatu, choimbira chazingwe, chitoliro chathumba ndi zipangizo zina zonse zoimbira, zili bwino. Koma mukakana kulambira, nthawi yomweyo muponyedwa mungʼanjo yoyaka moto. Ndipo ndi mulungu uti amene angakupulumutseni mʼmanja mwanga?”+

  • Danieli
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 3:15

      Ulosi wa Danieli, ptsa. 75-77

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena