-
Danieli 5:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Ndiyeno anabweretsa ziwiya zagolide zimene anazitenga mʼkachisi, mʼnyumba ya Mulungu ku Yerusalemu. Kenako mfumuyo, nduna zake, adzakazi ake ndi akazi ake ena anayamba kumwera mʼziwiyazo.
-