Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pa nthawiyo, nduna zapamwamba ndi masatarapi aja ankafufuza zifukwa zoti amuimbire mlandu Danieli pa nkhani zokhudza mmene ankayendetsera zinthu mu ufumuwo. Koma iwo sanapeze chifukwa chilichonse chomuimbira mlandu kapena chinthu chilichonse chachinyengo chimene anachita. Zinali choncho chifukwa Danieli anali wokhulupirika ndipo iwo anapeza kuti sankanyalanyaza udindo wake kapena kuchita zachinyengo zilizonse.

  • Danieli
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 6:4

      Ulosi wa Danieli, ptsa. 116-117, 124-125

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena