Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 10:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndiyeno munthu uja anandiuza kuti: “Iwe Danieli, usachite mantha.+ Mawu ako akhala akumveka kuyambira tsiku loyamba pamene unatsegula mtima wako kuti umvetse tanthauzo la zinthu zimenezi, ndiponso pamene unadzichepetsa pamaso pa Mulungu wako, ndipo ine ndabwera chifukwa cha mawu akowo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena