-
Hoseya 2:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 Ndidzawononga mitengo yake ya mpesa ndi ya mkuyu imene iye wanena kuti:
“Amenewa ndi malipiro amene amuna ondikonda kwambiri anandipatsa.”
Koma ine mitengoyo ndidzaisandutsa kukhala nkhalango,
Ndipo zilombo zakutchire zidzaidya.
-