-
Mika 1:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Zifaniziro zake zonse zogoba zidzaphwanyidwa nʼkukhala zidutswazidutswa.+
Ndipo mphatso zonse zimene ankalandira ngati malipiro zidzatenthedwa pamoto.+
Mafano ake onse ndidzawawononga.
Chifukwa anawapeza kuchokera ku ndalama zimene ankalandira pochita uhule.
Ndipo tsopano zinthu zimenezi zidzatengedwa kuti zikakhale malipiro a mahule kwinakwake.”
-