Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mika 4:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Anthu ochokera mʼmitundu yosiyanasiyana adzabwera nʼkunena kuti:

      “Bwerani, tiyeni tipite kuphiri la Yehova,

      Tipite kunyumba ya Mulungu wa Yakobo.+

      Iye akatiphunzitsa njira zake,

      Ndipo ife tidzayenda mʼnjira zakezo.”

      Chifukwa chilamulo,* chidzaphunzitsidwa mu Ziyoni

      Ndipo mawu a Yehova adzaphunzitsidwa mu Yerusalemu.

  • Mika
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 4:2

      Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

      3/2016, tsa. 17

      Nsanja ya Olonda,

      8/15/2003, tsa. 17

      Lambirani Mulungu, ptsa. 6-7

      Galamukani!,

      12/8/1987, ptsa. 11-12

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena