Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mika 4:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mulungu adzaweruza mitundu yambiri ya anthu,+

      Ndipo adzakonza zinthu zolakwika zokhudza anthu ochokera mʼmitundu yamphamvu yakutali.

      Iwo adzasula malupanga awo kuti akhale makasu a pulawo,

      Ndiponso mikondo yawo kuti ikhale zida zosadzira mitengo.+

      Mtundu wa anthu sudzanyamula lupanga kuti umenyane ndi mtundu unzake,

      Ndipo anthuwo sadzaphunziranso nkhondo.+

  • Mika
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 4:3

      Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 45

      Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

      7/2017, tsa. 32

      Nsanja ya Olonda,

      11/1/2007, tsa. 15

      8/15/2003, tsa. 17

      3/1/1991, tsa. 19

      5/1/1989, tsa. 14

      Galamukani!,

      12/8/1987, ptsa. 11-12

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena