-
Zekariya 11:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Chifukwa ndilola kuti mʼdzikoli mukhale mʼbusa wina. Mʼbusa ameneyu sadzasamalira nkhosa zimene zikuwonongeka.+ Iye sadzafunafuna nkhosa yaingʼono, sadzachiritsa yovulala+ komanso sadzapatsa chakudya nkhosa zimene zikadali zamphamvu. Mʼmalomwake adzadya nyama ya nkhosa yonenepa+ ndipo adzakupula* ziboda za nkhosazo.+
-