Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 2:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndiyeno Herode ataona kuti okhulupirira nyenyezi aja amupusitsa, anakwiya koopsa. Choncho anatumiza anthu kukapha ana onse aamuna mʼBetelehemu ndi mʼzigawo zake zonse, kuyambira azaka ziwiri kutsika mʼmunsi. Anasankha kupha ana a zaka zimenezi mogwirizana ndi zimene okhulupirira nyenyezi aja anamuuza.+

  • Mateyu
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 2:16

      Yesu—Ndi Njira, tsa. 24

      Nsanja ya Olonda,

      8/15/2011, tsa. 10

  • 1. Kuwala Kwenikweni kwa Dziko
    Malifalensi a Mavidiyo a Uthenga Wabwino wa Yesu
    • Herode anapha ana onse aamuna ku Betelehemu komanso m’zigawo zake zonse (gnj 1 57:35–59:32)

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena