Mateyu 6:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Koma iwe ukamapemphera, uzilowa mʼchipinda chako nʼkutseka chitseko ndipo uzipemphera kwa Atate wako amene sungathe kuwaona.+ Ukatero Atate wako amene akuona zimene zikuchitika ngakhale kuti iweyo sungathe kuwaona, adzakubwezera. Mateyu Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 6:6 Yesu—Ndi Njira, tsa. 88 Nsanja ya Olonda,10/1/2010, tsa. 92/15/2009, tsa. 162/1/2007, tsa. 197/15/1996, tsa. 67/15/1990, tsa. 6
6 Koma iwe ukamapemphera, uzilowa mʼchipinda chako nʼkutseka chitseko ndipo uzipemphera kwa Atate wako amene sungathe kuwaona.+ Ukatero Atate wako amene akuona zimene zikuchitika ngakhale kuti iweyo sungathe kuwaona, adzakubwezera.
6:6 Yesu—Ndi Njira, tsa. 88 Nsanja ya Olonda,10/1/2010, tsa. 92/15/2009, tsa. 162/1/2007, tsa. 197/15/1996, tsa. 67/15/1990, tsa. 6