-
Mateyu 21:43Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
43 Nʼchifukwa chake ndikukuuzani kuti, Ufumu wa Mulungu udzachotsedwa kwa inu nʼkuperekedwa ku mtundu wobereka zipatso zake.
-