-
Mateyu 27:19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 Komanso atakhala pampando woweruzira milandu, mkazi wake anamutumizira uthenga wakuti: “Nkhani ya munthu wolungamayu isakukhudzeni chifukwa ine ndavutika kwambiri lero ndi maloto okhudza iyeyu.”
-