-
Mateyu 28:9Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 Mwadzidzidzi Yesu anakumana nawo nʼkunena kuti: “Moni azimayi!” Kenako iwo anafika pafupi nʼkugwira mapazi ake ndipo anamuweramira mpaka nkhope zawo pansi.
-