-
Maliko 14:70Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
70 Apanso Petulo anakana. Patapita kanthawi pangʼono, amene anali ataimirira chapafupi anayambanso kuuza Petulo kuti: “Ndithu iwenso uli mʼgulu la ophunzira ake. Ndipo ndiwenso Mgalileya.”
-