-
Luka 1:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 Ndiye tamvera! Udzakhala chete osatha kulankhula, mpaka tsiku limene zinthu zimenezi zidzachitike chifukwa sunakhulupirire mawu anga amene adzakwaniritsidwe pa nthawi yake imene inaikidwiratu.”
-
-
1. Kuwala Kwenikweni kwa DzikoMalifalensi a Mavidiyo a Uthenga Wabwino wa Yesu
-
-
Gabirieli ananeneratu za kubadwa kwa Yohane M’batizi (gnj 1 06:04–13:53)
-