-
Luka 2:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Mʼdera limeneli munalinso abusa amene ankagonera kumalo odyetsera ziweto nʼkumayangʼanira nkhosa zawo usiku wonse.
-
-
1. Kuwala Kwenikweni kwa DzikoMalifalensi a Mavidiyo a Uthenga Wabwino wa Yesu
-
-
Angelo anaonekera kwa abusa ali kutchire (gnj 1 39:54–41:40)
-