-
Luka 2:37Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
37 Tsopano anali mkazi wamasiye ndipo anali ndi zaka 84 koma sankasowa pakachisi. Ankachita utumiki wopatulika masana ndi usiku ndipo ankasala kudya komanso kupemphera mopembedzera.
-
-
1. Kuwala Kwenikweni kwa DzikoMalifalensi a Mavidiyo a Uthenga Wabwino wa Yesu
-
-
Anna analankhula zokhudza mwanayo (gnj 1 48:52–50:21)
-