Luka 12:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Kenako anauza ophunzira ake kuti: “Nʼchifukwa chake ndikukuuzani kuti, siyani kudera nkhawa za moyo wanu kuti mudzadya chiyani kapena kudera nkhawa za matupi anu kuti mudzavala chiyani.+ Luka Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 12:22 Yesu—Ndi Njira, ptsa. 180-181 Nsanja ya Olonda,9/15/1988, tsa. 9
22 Kenako anauza ophunzira ake kuti: “Nʼchifukwa chake ndikukuuzani kuti, siyani kudera nkhawa za moyo wanu kuti mudzadya chiyani kapena kudera nkhawa za matupi anu kuti mudzavala chiyani.+