6 Pa nthawi imeneyo, pamene ophunzirawo ankapitiriza kuwonjezeka, Ayuda olankhula Chigiriki anayamba kudandaula za Ayuda olankhula Chiheberi. Ankadandaula chifukwa akazi amasiye a Chigiriki ankanyalanyazidwa pa nkhani yogawa chakudya cha tsiku ndi tsiku.+