-
Machitidwe 14:14Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 Koma atumwiwo, Baranaba ndi Paulo, atamva zimenezi anangʼamba malaya awo akunja nʼkuthamanga kukalowa mʼgulu la anthu lija akufuula kuti:
-