2 Akorinto 1:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Chifukwa ndinkafuna kuti ndikamapita ku Makedoniya ndidzadutsire kwanuko kudzakuchezerani, ndipo ndikadzachoka ku Makedoniya ndidzabwerenso kwanuko kenako mudzandiperekeze popita ku Yudeya.+ 2 Akorinto Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 1:16 Nsanja ya Olonda,3/15/2014, ptsa. 30-3110/15/2012, tsa. 29
16 Chifukwa ndinkafuna kuti ndikamapita ku Makedoniya ndidzadutsire kwanuko kudzakuchezerani, ndipo ndikadzachoka ku Makedoniya ndidzabwerenso kwanuko kenako mudzandiperekeze popita ku Yudeya.+