-
Akolose 2:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Ndikuchita zimenezi kuti mitima yawo ilimbikitsidwe+ ndiponso kuti onse akhale ogwirizana mʼchikondi+ komanso kuti alandire chuma chonse chimene chimabwera chifukwa chomvetsa bwino zinthu, popanda kukayikira chilichonse, nʼcholinga choti adziwe molondola chinsinsi chopatulika cha Mulungu, chomwe ndi Khristu.+
-