-
1 Timoteyo 6:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 Menya nkhondo yabwino ya chikhulupiriro. Gwira mwamphamvu moyo wosatha umene anakuitanira. Paja unalengeza momveka bwino zokhudza moyo umenewu pamaso pa mboni zambiri.
-