13 Ndiyeno ndinaona chiwombankhanga chikuuluka pafupi mumlengalenga ndipo ndinamva chikulankhula ndi mawu okweza akuti: “Tsoka, tsoka, tsoka+ kwa amene akukhala padziko lapansi, chifukwa cha kulira kwa malipenga otsalawo, amene angelo atatu atsala pangʼono kuwaliza!”+