Chivumbulutso 16:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Mzinda waukulu+ unagawika zigawo zitatu ndipo mizinda ya mitundu ya anthu inagwa. Ndiyeno Mulungu anakumbukira Babulo Wamkulu,+ kuti amupatse kapu imene inali ndi vinyo wa mkwiyo wake waukulu.+ Chivumbulutso Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 16:19 Mapeto a Chivumbulutso, tsa. 234
19 Mzinda waukulu+ unagawika zigawo zitatu ndipo mizinda ya mitundu ya anthu inagwa. Ndiyeno Mulungu anakumbukira Babulo Wamkulu,+ kuti amupatse kapu imene inali ndi vinyo wa mkwiyo wake waukulu.+