Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Chivumbulutso 17:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Chilombo chimene waona, chinalipo, koma panopa kulibe, komabe chatsala pangʼono kutuluka kuphompho,+ ndipo chipita kuchiwonongeko. Anthu amene akukhala padziko lapansi, amene mayina awo sanalembedwe mumpukutu wa moyo+ kuyambira pamene dziko linakhazikitsidwa, adzadabwa kwambiri akadzaona kuti chilombocho chinalipo, panopa kulibe, koma chidzakhalaponso.

  • Chivumbulutso
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 17:8

      Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

      Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

      5/2022, tsa. 10

      Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 247-251

      Nsanja ya Olonda,

      6/1/1988, ptsa. 27-28

      9/1/1987, ptsa. 20, 29

      2/1/1986, tsa. 7

      Galamukani!,

      11/8/1987, tsa. 28

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena