Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 30:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Kenako, Yakobo anachotsapo nkhosa zamphongo zing’onozing’ono n’kuziika pazokha. Atatero, anapatula nkhosa zonse zamizeremizere ndi zofiirira zimene zinali pakati pa ziweto za Labani. Kenako anatembenuza nkhosa zotsalazo kuti ziyang’ane zamizeremizere ndi zofiirira zija. Iye anaika ziweto zake pazokha, ndipo sanaziphatikize ndi ziweto za Labani.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena