26 Koma Mose anati: “Sikoyenera kuchita zimenezo, chifukwa mwina chinthu chomwe tingapereke nsembe kwa Yehova Mulungu wathu chingakhale chonyansa kwa Aiguputo.+ Kodi Aiguputo sadzatiponya miyala ngati tingapereke nsembe chinthu chonyansa pamaso pawo?