-
Nyimbo ya Solomo 8:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 “Munda wanga wa mpesa ndingathe kuchita nawo chilichonse. Ndalama 1,000 zasilivazo ndi zanu inu a Solomo, ndipo ndalama zasiliva 200 ndi za anthu amene amatenga zipatso za munda wanu wa mpesa.”
-