18 Phindu lake ndi malipiro ake+ zidzakhala zopatulika kwa Yehova. Phindu lakelo silidzasungidwa kapena kukundikidwa chifukwa malipiro ake adzakhala a anthu okhala pamaso pa Yehova,+ kuti anthuwo azidya mpaka kukhuta ndiponso kuti azivala zovala zokongola.+