Yesaya 50:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, adzandithandiza. Ndani amene anganene kuti ndine wolakwa?+ Onsewo adzatha ngati chovala.+ Njenjete* idzawadya.+ Yesaya Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 50:9 Nsanja ya Olonda,1/15/2009, tsa. 22 Yesaya 2, ptsa. 161-163
9 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, adzandithandiza. Ndani amene anganene kuti ndine wolakwa?+ Onsewo adzatha ngati chovala.+ Njenjete* idzawadya.+