6 Anatenga amuna amphamvu, akazi awo, ana aang’ono, ana aakazi a mfumu+ ndiponso aliyense amene Nebuzaradani+ mkulu wa asilikali olondera mfumu analola kuti akhale ndi Gedaliya+ mwana wa Ahikamu,+ mwana wa Safani.+ Anatenganso mneneri Yeremiya ndi Baruki+ mwana wa Neriya.